LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • CO-pgm23 masa. 4-5
  • Tsiku Laciŵili

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tsiku Laciŵili
  • Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2023
  • Nkhani Zofanana
  • Tsiku Loyamba
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2023
  • Tsiku Laciŵili
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2021
  • Tsiku Laciŵili
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2017
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2024
Onaninso Zina
Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2023
CO-pgm23 masa. 4-5
Zithunzi: Mfundo zazikulu za Tsiku Laciŵili. 1. Banja likuceza mwacimwemwe pa vidiyo. 2. Mfumu isinkhasinkha. 3. Tate na mwana wake kumsika.

Tsiku Laciŵili

“Khalani oleza mtima kwa onse” 1 Atesalonika 5:14

M’maŵa

  • 8:20 Vidiyo ya Nyimbo

  • 8:30 Nyimbo Na. 58 na Pemphelo

  • 8:40 YOSIYILANA: “Timasonyeza Kuti Ndife Atumikia Mulungu . . . Mwa Kukhala Oleza Mtima”

    • • Pamene Tilalikila (Machitidwe 26:29; 2 Akorinto 6:4, 6)

    • • Potsogoza Maphunzilo a Baibo (Yohane 16:12)

    • • Polimbikitsana Wina na Mnzake (1 Atesalonika 5:11)

    • • Mukamatumikila Monga Mkulu (2 Timoteyo 4:2)

  • 9:30 Inu Amene Mwaonetsedwa Kuleza Mtima, Onetsani Kuleza Mtima! (Mateyu 7:1, 2; 18:23-35)

  • 9:50 Nyimbo Na. 138 na Zilengezo

  • 10:00 YOSIYILANA: ‘Moleza Mtima, PitilizaniKulolelana m’Cikondi’

    • • Acibale Amene si Mboni (Akolose 4:6)

    • • Mnzanu wa mu Ukwati (Miyambo 19:11)

    • • Ana Anu (2 Timoteyo 3:14)

    • • Acibale Odwala Kapena Okalamba (Aheberi 13:16)

  • 10:45 UBATIZO: Kuleza Mtima kwa Yehova Ni Cipulumutso Cathu! (2 Petulo 3:13-15)

  • 11:15 Nyimbo Na. 75 na Zilengezo

Masana

  • 12:35 Vidiyo ya Nyimbo

  • 12:45 Nyimbo Na. 106

  • 12:50 Samalani na Mtima Wongofuna KudzisangalatsaNthawi Yomweyo (1 Atesalonika 4:3-5; 1 Yohane 2:17)

  • 13:15 YOSIYILANA: “Woleza Mtima ni WabwinoKuposa Munthu Wodzikuza”

    • • Tengelani Abele, Osati Adamu (Mlaliki 7:8)

    • • Tengelani Yakobo, Osati Esau (Aheberi 12:16)

    • • Tengelani Mose, Osati Kora (Numeri 16:9, 10)

    • • Tengelani Samueli, Osati Sauli (1 Samueli 15:22)

    • • Tengelani Yonatani, Osati Abisalomu (1 Samueli 23:16-18)

  • 14:15 Nyimbo Na. 87 na Zilengezo

  • 14:25 SEŴELO: ‘Lola Yehova AkutsogolelePanjila Yako’—Gawo 1 (Salimo 37:5)

  • 14:55 ‘Pozunzidwa, Timapilila Moleza Mtima’ (1 Akorinto 4:12; Aroma 12:14, 21)

  • 15:30 Nyimbo Na. 79 na Pemphelo Lothela

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani