Tsiku Laciŵili
“Khalani oleza mtima kwa onse” 1 Atesalonika 5:14
M’maŵa
- 8:20 Vidiyo ya Nyimbo 
- 8:30 Nyimbo Na. 58 na Pemphelo 
- 8:40 YOSIYILANA: “Timasonyeza Kuti Ndife Atumikia Mulungu . . . Mwa Kukhala Oleza Mtima” - • Pamene Tilalikila (Machitidwe 26:29; 2 Akorinto 6:4, 6) 
- • Potsogoza Maphunzilo a Baibo (Yohane 16:12) 
- • Polimbikitsana Wina na Mnzake (1 Atesalonika 5:11) 
- • Mukamatumikila Monga Mkulu (2 Timoteyo 4:2) 
 
- 9:30 Inu Amene Mwaonetsedwa Kuleza Mtima, Onetsani Kuleza Mtima! (Mateyu 7:1, 2; 18:23-35) 
- 9:50 Nyimbo Na. 138 na Zilengezo 
- 10:00 YOSIYILANA: ‘Moleza Mtima, PitilizaniKulolelana m’Cikondi’ - • Acibale Amene si Mboni (Akolose 4:6) 
- • Mnzanu wa mu Ukwati (Miyambo 19:11) 
- • Ana Anu (2 Timoteyo 3:14) 
- • Acibale Odwala Kapena Okalamba (Aheberi 13:16) 
 
- 10:45 UBATIZO: Kuleza Mtima kwa Yehova Ni Cipulumutso Cathu! (2 Petulo 3:13-15) 
- 11:15 Nyimbo Na. 75 na Zilengezo 
Masana
- 12:35 Vidiyo ya Nyimbo 
- 12:45 Nyimbo Na. 106 
- 12:50 Samalani na Mtima Wongofuna KudzisangalatsaNthawi Yomweyo (1 Atesalonika 4:3-5; 1 Yohane 2:17) 
- 13:15 YOSIYILANA: “Woleza Mtima ni WabwinoKuposa Munthu Wodzikuza” - • Tengelani Abele, Osati Adamu (Mlaliki 7:8) 
- • Tengelani Yakobo, Osati Esau (Aheberi 12:16) 
- • Tengelani Mose, Osati Kora (Numeri 16:9, 10) 
- • Tengelani Samueli, Osati Sauli (1 Samueli 15:22) 
- • Tengelani Yonatani, Osati Abisalomu (1 Samueli 23:16-18) 
 
- 14:15 Nyimbo Na. 87 na Zilengezo 
- 14:25 SEŴELO: ‘Lola Yehova AkutsogolelePanjila Yako’—Gawo 1 (Salimo 37:5) 
- 14:55 ‘Pozunzidwa, Timapilila Moleza Mtima’ (1 Akorinto 4:12; Aroma 12:14, 21) 
- 15:30 Nyimbo Na. 79 na Pemphelo Lothela