LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • CO-pgm23 masa. 6-7
  • Tsiku Lacitatu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tsiku Lacitatu
  • Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2023
  • Nkhani Zofanana
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2021
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2024
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2022
  • Tsiku Lacitatu
    Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2020
Onaninso Zina
Pulogilamu ya Msonkhano Wacigawo wa mu 2023
CO-pgm23 masa. 6-7
Zithunzi: Mfundo zazikulu za Tsiku Lacitatu. 1. Mwamuna na mkazi wake m’sitima. 2. Mneneli. 3. Tate, mayi, na mwana wawo wacitsikana, akukambilana pamene akupumula m’mbali mwa msewu.

Tsiku Lacitatu

“Yehova azidzayembekezela kuti akukomeleni mtima” Yesaya 30:18

M’maŵa

  • 8:20 Vidiyo ya Nyimbo

  • 8:30 Nyimbo Na. 95 na Pemphelo

  • 8:40 YOSIYILANA: Citsanzo ca Kuleza Mtima Cimene Tingatengele—Aneneli

    • • Eliya (Yakobo 5:10, 17, 18)

    • • Mika (Mika 7:7)

    • • Hoseya (Hoseya 3:1)

    • • Yesaya (Yesaya 7:3)

    • • Ezekieli (Ezekieli 2:3-5)

    • • Yeremiya (Yeremiya 15:16)

    • • Danieli (Danieli 9:22, 23)

  • 10:05 Nyimbo Na. 142 na Zilengezo

  • 10:15 NKHANI YA ANTHU ONSE: Kodi Mulungu Adzacitapo Kanthu Kuti Akuthandizeni? (Yesaya 64:4)

  • 10:45 Cidule ca Nsanja ya Mlonda

  • 11:15 Nyimbo Na. 94 na Kupumula

Masana

  • 12:35 Vidiyo ya Nyimbo

  • 12:45 Nyimbo Na. 114

  • 12:50 SEŴELO: ‘Lola Yehova Akutsogolele Panjila Yako’—Gawo 2 (Salimo 37:5)

  • 13:30 Nyimbo Na. 115 na Zilengezo

  • 13:40 Yehova Akuyembekezela Moleza Mtima Kuti Akuonetseni Kukoma Mtima (Yesaya 30:18-21; 60:17; 2 Mafumu 6:15-17; Aefeso 1:9, 10)

  • 14:40 Nyimbo Yatsopano na Pemphelo Lothela

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani