LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 10/13 tsa. 3
  • Kodi Mudzacita Ciani Panthawi ya Maholide?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mudzacita Ciani Panthawi ya Maholide?
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Nkhani Zofanana
  • Onetsani Kuti Mumacilikiza Kulambila Koona
    Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni
  • Kodi Zikondwelelo Zonse Zimam’sangalatsa Mulungu?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • Sankhani Kulambila Mulungu
    Zimene Baibulo Ingatiphunzitse
  • Kodi Tiyenela Kukondwelela Maholide?
    Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni
Onaninso Zina
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 10/13 tsa. 3

Kodi Mudzacita Ciani Panthawi ya Maholide?

Popeza kuti anthu ambili amakhala panyumba panthawi ya maholide acipembedzo ndi maholide ena, imeneyi imakhala nthawi yabwino yolalikila. Mipingo ikulimbikitsidwa kupanga makonzedwe apadela kuti ikalalikile panthawi ya maholide. Popeza kuti anthu ambili m’gawo aziuka mocedwa, ndi bwino kusintha nthawi yokonzekela kupita mu ulaliki. Ngati n’kotheka, pa Msonkhano wa Nchito mungapeleke cilengezo codziŵitsa mpingo za makonzedwe apadela ocita umboni panthawi ya maholide. Limbikitsani onse amene angathe kuti atengeko mbali pa nchito yocitila umboni. N’zoona kuti maholide amatipatsa mpata wopuma ndi kucita zinthu zaumwini. Koma m’malo mongothela tsiku lonse kucita zinthu zosangulutsa, bwanji osapatula nthawi yocitako ulaliki? Mukacita zimenezi, mudzakhala ndi cimwemwe cimene cimabwela kaamba kocita utumiki wopatulika.—Mat. 11:29, 30.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani