LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 September tsa. 1
  • Maulaliki a Citsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maulaliki a Citsanzo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Tumitu
  • Nkhani Zofanana
  • NSANJA YA MLONDA
  • NSANJA YA MLONDA (cikuto cothela)
  • Lemba: Dan. 2:44
  • PHUNZITSANI COONADI
  • Lemba: 1 Pet. 5:7
  • KONZANI ULALIKI WANU
  • Maulaliki Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Maulaliki Acitsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Maulaliki a Citsanzo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 September tsa. 1
Mlongo alalikila mayi ndi mwana wake ku West Bengal m’dziko la India

Alalikila mayi ndi mwana wake ku West Bengal m’dziko la India

Maulaliki a Citsanzo

NSANJA YA MLONDA

Nsanja ya Mlonda Na. 5 2016 | Kodi Tingapeze Kuti Citonthozo?

Funso: Aliyense amafuna citonthozo nthawi zina. Kodi n’kuti kumene tingacipeze?

Lemba: 2 Akor. 1:3, 4

Cogaŵila: Magazini iyi ya Nsanja ya Mlonda ifotokoza mmene Mulungu amatitonthozela.

NSANJA YA MLONDA (cikuto cothela)

Funso: Anthu ena amaganiza kuti Ufumu wa Mulungu ni mtima wa munthu. Ena amaganiza kuti ndi mtendele umene anthu adzabweletsa padziko lonse. Inu muganiza bwanji?

Lemba: Dan. 2:44

Cogaŵila: Baibulo imakamba kuti Ufumu wa Mulungu ndi boma lenileni. Nkhani iyi ifotokoza zinthu zina zambili zimene Baibulo imakamba ponena za Ufumu wa Mulungu.

PHUNZITSANI COONADI

Baibulo lotsegula

Funso: Tidziŵa bwanji kuti Mulungu amatidela nkhawa?

Lemba: 1 Pet. 5:7

Mfundo ya Coonadi: Mulungu amafuna kuti tizipemphela kwa iye cifukwa amatidela nkhawa.

KONZANI ULALIKI WANU

Funso:

Lemba:

Cogaŵila:

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani