LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 July tsa. 4
  • Kodi Mumadziimbabe Mlandu?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mumadziimbabe Mlandu?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Khalanibe Okhulupilika Pamene M’bululu Wanu Wacotsedwa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Laibulali Imene Mungathe Kuinyamula Kumanja
    Mmene Zopeleka Zanu Zimagwilila Nchito
  • Kodi Mukugwilitsila Nchito JW Laibulale?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Mmene Tingaseŵenzetsele JW Laibulale
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 July tsa. 4

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kodi Mumadziimbabe Mlandu?

Kungakhale kovuta kuleka kudziimba mlandu pa zolakwa zimene Yehova anatikhululukila kale. Nkhani imeneyi inakambiwa pa msonkhano wa cigawo wa mu 2016 wa mutu wakuti “Khalanibe Wokhulupilika kwa Yehova.” Ndipo tinatamba vidiyo yokhudza zimenezi. Seŵenzetsani JW Library kuti mutambenso vidiyo imeneyo na kuyankha mafunso aya:

Makolo a Soniya amukumbatila
  • Kodi Soniya anakhala wocotsedwa kwa utali wanji?

  • Ni lemba liti limene akulu anamuŵelengela? Nanga inam’thandiza bwanji?

  • Soniya atabwezedwa, kodi mpingo unamulandila bwanji?

  • Ni maganizo ati amene Soniya analimbana nawo, nanga atate ake anam’thandiza bwanji?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani