LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb21 July tsa. 10
  • Mmene Cilamulo Cinaonetsela Kuti Yehova Amawadela Nkhawa Akazi

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mmene Cilamulo Cinaonetsela Kuti Yehova Amawadela Nkhawa Akazi
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Yehova Amafuna Kuti Tizimulambila Motani?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Mfundo Zothandiza Kuweluza Milandu Mwacilungamo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Mmene Cilamulo Cinaonetsela Kuti Yehova Amadela Nkhawa Osauka
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
  • Funani Citetezo M’manja a Yehova “Amene Adzakhalapo Mpaka Kale-kale”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
mwb21 July tsa. 10
Mayi waciisiraeli akunkha tiligu m’munda.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Mmene Cilamulo Cinaonetsela Kuti Yehova Amawadela Nkhawa Akazi

Mwamuna akakwatila sanayenele kupita kunkhondo n’kusiya mkazi wake m’caka coyamba ca ukwati wawo (Deut. 24:5; it-2 1196 ¶4)

Akazi amasiye anali kusamalidwa mwakuthupi (Deut. 24:19-21; it-1 963 ¶2)

Akazi amasiye amene analibe ana anali kupatsidwa mwayi wokwatiwa kuti abeleke ana (Deut. 25:5, 6; w11 3/1 23)

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi m’banja langa kapena mu mpingo, ningaonetse bwanji kuti akazi nimaaganizila?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani