LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 July tsa. 16
  • Kampeni Yapadela Yolengeza Ufumu wa Mulungu mu September!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kampeni Yapadela Yolengeza Ufumu wa Mulungu mu September!
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Kampeni Yapadela Yolengeza za Ufumu wa Mulungu mu November
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Kampeni Yapadela Yoyambitsa Maphunzilo a Baibo mu September
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Mipata Yoonjezeka Yotamanda Yehova
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Lalikilani Uthenga Wabwino Wakuti Dziko Labwino Lili Pafupi!
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 July tsa. 16
Yesu wakhala pampando wacifumu kumwamba. Iye akulamulila dziko lapansi la paladaiso monga Mfumu.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Kampeni Yapadela Yolengeza Ufumu wa Mulungu mu September!

M’mwezi wa September, tidzakhala na nchito yapadela yolengeza mwakhama za Ufumu wa Mulungu kuti ndiwo njila yokha yothetsela mavuto a anthu. (Mat. 24:14) Kodi mungatengeko mbali motani pa nchitoyi? Mukaŵelenge lemba lokamba za Ufumu wa Mulungu kwa anthu ambili mmene mungathele m’mwezi umenewo. Ngati winawake waonetsa cidwi, mugaŵileni Nsanja ya Mlonda yogaŵila ya Na. 2 2020. Mukatelo, mukabweleleko mwamsanga, ndipo mukayesetse kuyambitsa phunzilo la Baibo poseŵenzetsa bulosha yakuti Kondwelani na Moyo Kwamuyaya! Onse amene adzacita upainiya wothandiza mu September adzakhala na ufulu wolalikila maola 15 kapena 30.

“Nsanja ya Mlonda” Na. 2 2020, ya mutu wakuti “Kodi Ufumu wa Mulungu n’Ciani?”

Posacedwa, Ufumu wa Mulungu udzaphwanya maufumu onse otsutsana nawo. (Dan. 2:44; 1 Akor. 15:24, 25) Conco, tiyeni tiuseŵenzetse mokwanila mwayi wapadela umenewu, poonetsa kuti ndife okhulupilika kwa Yehova na Ufumu wake!

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani