LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 50
  • Pemphelo Langa Lodzipelekela kwa Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pemphelo Langa Lodzipelekela kwa Mulungu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Pemphero Langa Losonyeza Kudzipereka
    Imbirani Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova mwa Kuimba Nyimbo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 50

NYIMBO 50

Pemphelo Langa Lodzipelekela kwa Mulungu

Yopulinta

(Mateyu 22:37)

  1. 1. Tengani mtima wanga,

    Uzikonda co’nadi.

    Tengani mau anga,

    Aimbe motamanda.

  2. 2. Tengani manja anga;

    Agwile nchito yanu.

    Tengani cuma canga,

    Cikutumikileni.

  3. 3. Tengani moyo wanga,

    Ine nadzipeleka.

    Zocita zanga zonse

    Zikukondweletseni.

(Onaninso Sal. 40:8; Yoh. 8:29; 2 Akor. 10:5.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani