LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 76
  • Kodi Mumamvela Bwanji?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mumamvela Bwanji?
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Mumamvela Bwanji?
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Yehova Alangiza Mwacikondi Kuti: “Mwana Wanga, Khala Wanzelu”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • ‘Tsimikizilani Zinthu Zofunika Kwambili’
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tinadzipeleka kwa Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 76

NYIMBO 76

Kodi Mumamvela Bwanji?

Yopulinta

(Aheberi 13:15)

  1. 1. Mumamvela bwanji,

    polalikila ena,

    Na kuphunzitsa anthu

    okonda co’nadi?

    Ngati simuleka,

    M’lungu adzadalitsa.

    Mudzathandiza anthu

    kudziŵa Yehova.

    (KOLASI)

    Ise timasangalala

    kudzipeleka kwa M’lungu.

    Ndiponso sitidzaleka

    Kum’tamanda iye.

  2. 2. Mumamvela bwanji

    kuona kuti anthu

    Akumvetsela uthenga

    wopatsa moyo?

    Ena amakana,

    safuna na kumvela.

    Koma ise sitileka

    kulalikila.

    (KOLASI)

    Ise timasangalala

    kudzipeleka kwa M’lungu.

    Ndiponso sitidzaleka

    Kum’tamanda iye.

  3. 3. Mumamvela bwanji

    kuona kuti M’lungu,

    Adzakuthandizani

    kuti mupambane?

    Timalalikila

    na kuphunzitsa anthu,

    Tifuna kuti

    nawo akapulumuke.

    (KOLASI)

    Ise timasangalala

    kudzipeleka kwa M’lungu.

    Ndiponso sitidzaleka

    Kum’tamanda iye.

(Onaninso Mac. 13:48; 1 Ates. 2:4; 1 Tim. 1:11.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani