LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 38
  • Adzakulimbitsa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Adzakulimbitsa
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Mulungu Adzakupatsani Mphamvu
    Imbirani Yehova
  • Tikhale na Cikhulupililo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 38

NYIMBO 38

Adzakulimbitsa

Yopulinta

(1 Petulo 5:10)

  1. 1. Panali cifukwa cimene Yehova,

    Anakupatsila coonadi.

    Anaona kuti unali kufuna,

    Kucita zinthu zom’kondweletsa.

    Unalonjeza kum’tumikila,

    Ndipo iye anakuthandiza.

    (KOLASI)

    Na magazi a Yesu, anakuombola.

    Adzakulimbitsa, nokupatsa mphamvu.

    Adzakutsogolela, na kukuteteza.

    Adzakulimbitsa, nokupatsa mphamvu.

  2. 2. Mwana wake Yesu anamupeleka,

    Afuna zinthu zikuyendele.

    Anamupeleka Yesu mwacikondi,

    Conco Iye adzakulimbitsa.

    Cikondi cako sadzaiŵala.

    Amasamala za anthu ake.

    (KOLASI)

    Na magazi a Yesu, anakuombola.

    Adzakulimbitsa, nokupatsa mphamvu.

    Adzakutsogolela, na kukuteteza.

    Adzakulimbitsa, nokupatsa mphamvu.

(Onaninso Aroma 8:32; 14:8, 9; Aheb. 6:10; 1 Pet. 2:9.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani