LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 December tsa. 6
  • Kodi Cikwati Canu Cimakondweletsa Yehova?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Cikwati Canu Cimakondweletsa Yehova?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Nkhani Zofanana
  • Pambuyo Pa Tsiku La Cikwati
    Mmene Tingakhalilebe mu Cikondi ca Mulungu
  • Khalani Okhulupilika kwa Wina ndi Mnzake
    N’zotheka Banja Lanu Kukhala Lacimwemwe
  • Cikwati—Ciyambi na Cifuno Cake
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • Muzilemekeza “Cimene Mulungu Wacimanga Pamodzi”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 December tsa. 6
Mwamuna waciisiraeli akusiya mkazi wake

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MALAKI 1-4

Kodi Cikwati Canu Cimakondweletsa Yehova?

2:13-16

  • M’nthawi ya Malaki, Aisiraeli ambili anali kusudzulana pa zifukwa zopanda pake. Amene anali kucitila cinyengo anzawo a m’cikwati, kulambila kwawo kunali kosalandilika kwa Yehova

  • Yehova anadalitsa anthu olemekeza anzawo a m’cikwati

Kodi a m’cikwati angakhale bwanji okhulupilika . . .

  • m’maganizo?

  • pa zimene amaona?

  • m’zokamba zawo?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani