LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 87
  • Bwelani Mutsitsimulidwe!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Bwelani Mutsitsimulidwe!
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Bwerani Mudzatsitsimulidwe!
    Imbirani Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 87

NYIMBO 87

Bwelani Mutsitsimulidwe!

Yopulinta

(Aheberi 10: 24, 25)

  1. 1. Tili m’dziko la anthu osocela

    Iwo sadziŵa co’nadi.

    Kuti ’se tipewe njila zoipa,

    Tifunika citsogozo.

    Misonkhano imatitsitsimula,

    Imatilimbikitsadi.

    Itithandiza kukhulupilila

    Mwa Yehova M’lungu wathu.

    Conco ise sitidzataya konse

    Malamulo a Yehova.

    Misonkhano imatiphunzitsadi

    Kukondabe coonadi.

  2. 2. Yehova M’lungu ni Atate wathu;

    Timvele uphungu wake.

    Tizipatula nthawi yosonkhana

    Kuti tikhale anzelu.

    Polabadila akulu mu mpingo

    Ise ticita zabwino.

    Monga banja la m’cikhulupililo

    Mpingo umatithandiza.

    Conco pamene tiyembekezela

    Tsogolo lathu lowala,

    Tidzapitilizabe kuphunzila

    Nzelu zocoka kumwamba.

(Onaninso Sal. 37:18; 140:1; Miy. 18:1; Aef. 5:16; Yak. 3:17.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani