-
Yesaya 14:4-6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 mudzanena mwambi uwu wonyoza mfumu ya Babulo:
“Amene ankagwiritsa ntchito anzake mokakamiza uja wawonongedwa!
Kuponderezedwa kuja kwatha ndithu!+
-