Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb19.08 6
  • August 19-25

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • August 19-25
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19.08 6

August 19-25

AHEBERI 1-3

  • Nyimbo Na. 35 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Muzikonda Chilungamo Ndipo Muzidana ndi Kusamvera Malamulo”: (10 min.)

    • [Onerani vidiyo yakuti Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Aheberi.]

    • Aheb. 1:8​—Yesu akulamulira ndi “ndodo yachilungamo” (w14 2/15 5 ¶8)

    • Aheb. 1:9​—Yesu amakonda chilungamo ndipo amadana ndi kusamvera malamulo (w14 2/15 4-5 ¶7)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Aheb. 1:3​—Kodi Yesu wakhala akusonyeza ulemerero wofanana ndi wa Atate wake kuyambira kalekale? (it-1 1185 ¶1)

    • Aheb. 1:10-12​—N’chifukwa chiyani mtumwi Paulo anagwiritsa ntchito lemba la Salimo 102:25-27 ponena za Yesu Khristu? (it-1 1063 ¶7)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Aheb. 1:7-14 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Woyamba: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. (th phunziro 4)

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 5 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. M’patseni kapepala komuitanira kumisonkhano yathu, kenako musonyezeni vidiyo yakuti Kodi pa Nyumba ya Ufumu Pamachitika Zotani? koma musaonetse vidiyoyi. (th phunziro 11)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 121

  • Zofunika Pampingo: (15 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lvs 9:1-8

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 48 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani