Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 24:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Tsopano Abulahamu anali atakalamba ndipo anali ndi zaka zambiri. Yehova anali atamudalitsa m’chilichonse.+

  • Yobu 42:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova anadalitsa+ kwambiri mapeto a Yobu kuposa chiyambi chake+ moti iye anakhala ndi nkhosa 14,000, ngamila 6,000, ng’ombe 2,000 zimene zinkagwira ntchito zili ziwiriziwiri, ndi abulu aakazi 1,000.

  • Salimo 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.+

      Madalitso anu ali pa anthu anu.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 67:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Dziko lapansi lidzapereka zipatso zake.+

      Mulungu, ndithu Mulungu wathu, adzatidalitsa.+

  • Miyambo 10:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Madalitso a Yehova ndi amene amalemeretsa,+ ndipo sawonjezerapo ululu.+

  • Aheberi 6:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mwachitsanzo, nthaka imamwa madzi a mvula imene imagwera panthakapo kawirikawiri. Kenako imatulutsa zomera zimene zimapindulitsa amene ailima.+ Nthaka imeneyi imalandiranso dalitso kuchokera kwa Mulungu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena