Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 8:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Muzikumbukira Yehova Mulungu wanu, chifukwa ndiye amakupatsani mphamvu kuti mupeze chuma,+ pofuna kusunga pangano lake limene analumbirira makolo anu, monga mmene wachitira lero.+

  • 1 Samueli 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Yehova ndi Wopereka Umphawi+ ndi Wolemeretsa,+

      Wotsitsa ndiponso Wokweza,+

  • Salimo 37:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Anthu amene Mulungu akuwadalitsa adzalandira dziko lapansi,+

      Koma amene wawatemberera adzaphedwa.+

  • Salimo 107:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Mulungu amawadalitsa moti amachuluka kwambiri,+

      Ndipo salola kuti ng’ombe zawo zikhale zochepa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena