Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 25:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Pambuyo pa iyeyu, panabadwa m’bale wake, dzanja lake litagwira chidendene cha Esau,+ choncho Isaki anapatsa mwanayo dzina lakuti Yakobo.+ Pamene Rabeka amabereka anawa n’kuti Isaki ali ndi zaka 60.

  • Genesis 27:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Ndiyeno Esau anati: “Aka tsopano n’kachiwiri akundichenjerera amene uja!+ Kodi si chifukwa chake dzina lake ndi Yakobo?* Ukulu wanga anatenga kale,+ apa tsopano watenganso madalitso anga!”+ Iye anapitiriza kuti: “Kodi bambo, zoona palibiretu dalitso lililonse limene mwandisungirako?”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena