Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 31:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Aliyense amene mum’peze ndi milungu yanu aphedwe.+ Pamaso pa abale athuwa, fufuzani milungu yanuyo pa katundu wathu. Mukaipeza muitenge.”+ Koma Yakobo sanadziwe kuti Rakele anali ataba milunguyo.+

  • Genesis 37:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Kenako, iwo anatumiza mkanjo wamizeremizere uja kwa bambo awo. Atafika nawo anati: “Tapeza mkanjo uwu. Chonde, uonetsetseni+ kuti muone ngati uli mkanjo wa mwana wanu kapena ayi.”+

  • Levitiko 19:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “‘Musamaweruze mopanda chilungamo. Musamakondere munthu wosauka,+ ndiponso musamakondere munthu wolemera.+ Mnzako uzimuweruza mwachilungamo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena