Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 41:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Inuyo a Farao munatikwiyira kwambiri ife atumiki anu.+ Ineyo ndi mkulu wa ophika mkate munatitsekera m’ndende ya kunyumba kwa mkulu wa asilikali olondera mfumu.+

  • Miyambo 16:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mkwiyo wa mfumu umatanthauza amithenga a imfa,+ koma munthu wanzeru ndi amene amauziziritsa.+

  • Miyambo 19:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mkwiyo wa mfumu uli ngati kubangula kwa mkango wamphamvu,+ koma kukoma mtima kwake kuli ngati mame pazomera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena