Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 22:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pamapeto pake mfumu inauza Doegi+ kuti: “Iwe, tembenuka ukanthe ansembewa!” Nthawi yomweyo Doegi, Mwedomu,+ anatembenuka n’kukantha ndi kupha+ ansembewo tsiku limenelo, amuna 85 ovala efodi+ wa nsalu.

  • 1 Mafumu 2:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Kenako Mfumu Solomo inauzidwa kuti: “Yowabu wathawira kuchihema cha Yehova, ndipo ali pambali pa guwa lansembe.” Choncho Solomo anatuma Benaya mwana wa Yehoyada, kuti: “Pita ukamuphe!”+

  • Miyambo 19:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mkwiyo wa mfumu uli ngati kubangula kwa mkango wamphamvu,+ koma kukoma mtima kwake kuli ngati mame pazomera.+

  • Miyambo 20:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Kuopsa kwa mfumu kuli ngati kubangula kwa mkango wamphamvu.+ Aliyense woputa mkwiyo wake akuchimwira moyo wake womwe.+

  • Danieli 3:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pamenepo Nebukadinezara anapsa mtima kwambiri+ ndipo analamula kuti abweretse Sadirake, Mesake ndi Abedinego.+ Choncho anabweretsadi amuna amphamvu amenewa pamaso pa mfumu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena