Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 25:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndiyeno Esau anapempha Yakobo kuti: “Chonde, fulumira ndipatseko chakudya chofiiracho pang’ono, icho chofiiracho! Ndatopatu ine!” Ndiye chifukwa chake anatchedwa Edomu.*+

  • Genesis 36:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 mfumu Magidieli ndi mfumu Iramu. Amenewa ndiwo anali mafumu a Edomu+ monga mwa madera awo m’dziko lawo.+ Iyi ndiyo mibadwo ya Esau, kholo la Aedomu.+

  • Numeri 24:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Edomu adzalandidwa,+

      Ndithu Seiri+ adzalandidwa ndi adani ake,+

      Pamene Isiraeli akuonetsa kulimba mtima kwake.

  • 2 Mafumu 8:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Choncho Yehoramu anapita ku Zairi usiku pamodzi ndi magaleta ake onse. Kumeneko, iye ananyamuka usiku n’kukapha Aedomu amene anamuzungulira. Anaphanso akuluakulu oyang’anira asilikali okwera magaleta, ndipo anthu ena onse anathawira kumahema awo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena