Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 45:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kumeneko ndizidzakupatsani chakudya. Kwatsala zaka zisanu za njala,+ ndipo sindikufuna kuti inuyo ndi a m’nyumba yanu, ndi zonse zimene muli nazo muvutike ndi njala.”’

  • Genesis 47:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamenepo anthuwo anayamba kubweretsa ziweto zawo kwa Yosefe. Yosefeyo anali kuwapatsa chakudya mosinthana ndi mahatchi* awo, nkhosa, ng’ombe ndi abulu.+ M’chaka chonsecho, Yosefe anali kuwagawira chakudya mosinthana ndi ziweto zawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena