Genesis 7:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Chotero zamoyo zonse zoyenda padziko lapansi, monga zolengedwa zouluka, nyama zoweta, nyama zakutchire, ndiponso tizilombo tonse tambirimbiri toyenda padziko lapansi, zinafa+ pamodzi ndi anthu onse.+ Mlaliki 3:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Ndani akudziwa ngati mzimu* wa ana a anthu umakwera m’mwamba, ndiponso ngati mzimu wa zinyama umatsika pansi?+ Machitidwe 17:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Zoona, Mulungu analekerera nthawi ya kusadziwa koteroko,+ koma tsopano akuuza anthu kwina kulikonse kuti onse alape.+ 1 Akorinto 15:39 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 39 Mnofu sukhala wa mtundu umodzi, koma pali mnofu wa munthu, ndipo pali wa nyama, palinso wa mbalame, ndi winanso wa nsomba.+
21 Chotero zamoyo zonse zoyenda padziko lapansi, monga zolengedwa zouluka, nyama zoweta, nyama zakutchire, ndiponso tizilombo tonse tambirimbiri toyenda padziko lapansi, zinafa+ pamodzi ndi anthu onse.+
21 Ndani akudziwa ngati mzimu* wa ana a anthu umakwera m’mwamba, ndiponso ngati mzimu wa zinyama umatsika pansi?+
30 Zoona, Mulungu analekerera nthawi ya kusadziwa koteroko,+ koma tsopano akuuza anthu kwina kulikonse kuti onse alape.+
39 Mnofu sukhala wa mtundu umodzi, koma pali mnofu wa munthu, ndipo pali wa nyama, palinso wa mbalame, ndi winanso wa nsomba.+