Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 37:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Iwo anamuonera patali akubwera, ndipo asanafike pafupi anayamba kupangana chiwembu choti amuphe.+

  • Genesis 37:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tsopano amuna amalonda achimidiyani+ aja anali kudutsa mumsewu. Pamenepo abale a Yosefe anamutulutsa m’chitsimemo+ n’kumugulitsa kwa Aisimaeliwo. Anamugulitsa ndalama zasiliva 20,+ ndipo iwo anapita naye ku Iguputo.

  • Genesis 50:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 ‘Mukamuuze Yosefe kuti: “Chonde ndikukupempha, ukhululuke+ chiwembu cha abale ako, ndi kuchimwa kwawo pa zoipa zimene anakuchitira.”’+ Ndiye chonde, tikhululukireni ife akapolo a Mulungu wa bambo anu.”+ Atamuuza zimenezi, Yosefe analira kwambiri.

  • Machitidwe 7:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mitu ya mabanja ija inachitira nsanje+ Yosefe ndi kumugulitsa ku Iguputo.+ Koma Mulungu anali naye,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena