Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Iwe mwana wa munthu, Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wauza dziko la Isiraeli, kuti: ‘Mapeto! Mapeto afika kumalekezero anayi a dzikoli.+

  • Amosi 8:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno anandifunsa kuti: “Kodi ukuona chiyani+ Amosi?” Ndinayankha kuti: “Ndikuona dengu la zipatso za m’chilimwe.”+ Pamenepo Yehova anandiuza kuti: “Mapeto afika pa anthu anga Aisiraeli.+ Sindidzawamveranso chisoni.+

  • 1 Petulo 4:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma mapeto a zinthu zonse ayandikira.+ Choncho khalani oganiza bwino,+ ndipo khalani maso kuti musanyalanyaze kupemphera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena