Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 19:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Chotero, usiku uwunso anakhala akuwapatsa vinyo bambo awo kuti azimwa. Kenako, mwana wamng’ono uja anapita n’kukagona nawo. Koma kuyambira pamene mwanayo anabwera kudzagona nawo mpaka pamene anachoka, bambowo sanadziwe chilichonse.

  • Miyambo 23:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Udzati: “Andimenya koma sindinavulale, andikuntha koma sindinadziwe. Kodi ndidzuka nthawi yanji+ kuti ndikamwenso wina?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena