Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 39:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndiyeno anakonza miyala ya onekisi+ ndi kuiika m’zoikamo zagolide. Pamiyalayo analembapo mayina a ana a Isiraeli mochita kugoba ngati mmene amagobera chidindo.+

  • 2 Mbiri 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Choncho nditumizireni munthu waluso pa ntchito zagolide, zasiliva, zamkuwa,+ zachitsulo, ndiponso waluso pa ntchito za ubweya wa nkhosa wonyika mu utoto wofiirira, ulusi wofiira ndi wabuluu. Munthuyo akhalenso wodziwa kujambula ndi kulemba mochita kugoba, kuti adzagwire ntchito pamodzi ndi anthu aluso amene ndili nawo kuno ku Yuda ndi ku Yerusalemu, omwe Davide bambo anga anawasankha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena