Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Pamene Yakobo, kapena kuti Isiraeli anapita ku Iguputo, aliyense mwa ana ake aamuna anapitanso limodzi ndi banja lake. Mayina a ana a Yakobowo ndi awa:+

  • Ekisodo 28:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Utenge miyala iwiri ya onekisi+ ndi kulembapo+ mayina a ana a Isiraeli mochita kugoba.+

  • Ekisodo 28:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mayina 6 uwalembe pamwala umodzi ndipo mayina 6 otsalawo uwalembe pamwala winawo motsatira mmene anabadwira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena