Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 29:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ine ndakonzekera nyumba ya Mulungu wanga ndi mphamvu zanga zonse.+ Ndakonzekera+ golide+ wopangira zinthu zagolide, siliva wopangira zinthu zasiliva, mkuwa wopangira zinthu zamkuwa, zitsulo+ zopangira zinthu zachitsulo, ndi matabwa+ opangira zinthu zamatabwa. Ndakonzekeranso miyala ya onekisi,+ miyala yomanga ndi simenti yolimba, miyala yokongoletsera, miyala yamitundumitundu yamtengo wapatali, ndi miyala yambirimbiri ya alabasitala.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena