Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 6:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “Aroni ndi ana ake apereke nsembe+ iyi kwa Yehova monga nsembe yambewu: ufa wosalala+ wokwana gawo limodzi mwa magawo 10 a muyezo wa efa.+ Hafu imodzi m’mawa ndipo hafu inayo madzulo. Aliyense wa iwo azichita zimenezi nthawi zonse pa tsiku la kudzozedwa kwake.+

  • Levitiko 7:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ngati akupereka nsembeyo posonyeza kuyamikira,+ pamenepo azipereka nsembe yoyamikira pamodzi ndi mkate wozungulira woboola pakati, wopanda chofufumitsa, wothira mafuta. Aziperekanso timitanda ta mkate topyapyala topanda chofufumitsa, topaka mafuta,+ ndi mkate wozungulira woboola pakati, wothira mafuta, wophika ndi ufa wosalala wosakaniza bwino kwambiri ndi mafuta.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena