Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 22:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 “Mukafuna kupereka nsembe yoyamikira kwa Yehova+ muziipereka m’njira yakuti Mulungu akuyanjeni.

  • 2 Mbiri 29:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Pomalizira pake Hezekiya anati: “Tsopano mwayeneretsedwa kuti mukhale ansembe+ otumikira Yehova. Bweretsani nsembe zoyamikira+ ndi nsembe zina+ kunyumba ya Yehova.” Ndiyeno mpingowo unayamba kubweretsa nsembe zoyamikira ndi nsembe zina, ndipo aliyense wa mtima wofunitsitsa anali kubweretsa nsembe zopsereza.+

  • Nehemiya 12:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Pa tsiku limenelo anapereka nsembe zochuluka+ ndipo anasangalala+ pakuti Mulungu woona anawachititsa kusangalala kwambiri.+ Akazi+ ndi ana+ nawonso anasangalala, mwakuti phokoso la chisangalalo cha Yerusalemu linamveka kutali.+

  • Salimo 50:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pereka nsembe zoyamikira kwa Mulungu,+

      Ndipo pereka kwa Wam’mwambamwamba zimene walonjeza.+

  • 2 Akorinto 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mulungu akukudalitsani m’njira iliyonse kuti muthe kupereka mowolowa manja m’njira zosiyanasiyana, ndipo kudzera m’zochita zathu, kuwolowa manja koteroko kukuchititsa anthu kuyamika Mulunguyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena