-
2 Mbiri 29:31Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
31 Pomalizira pake Hezekiya anati: “Tsopano mwayeneretsedwa kuti mukhale ansembe+ otumikira Yehova. Bweretsani nsembe zoyamikira+ ndi nsembe zina+ kunyumba ya Yehova.” Ndiyeno mpingowo unayamba kubweretsa nsembe zoyamikira ndi nsembe zina, ndipo aliyense wa mtima wofunitsitsa anali kubweretsa nsembe zopsereza.+
-
-
Salimo 50:14Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
14 Pereka nsembe zoyamikira kwa Mulungu,+
Ndipo pereka kwa Wam’mwambamwamba zimene walonjeza.+
-