Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 32:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Zitatero Mose anati: “Dzilimbitseni* lero kuti muchite utumiki kwa Yehova,+ chifukwa aliyense wa inu waukira mwana wake ndi m’bale wake,+ kuti Mulungu akupatseni dalitso lero.”+

  • Levitiko 8:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Musachoke pakhomo la chihema chokumanako kwa masiku 7,+ kufikira tsiku lomaliza la kulongedwa kwanu unsembe, chifukwa kukupatsani mphamvu* kudzatenga masiku 7.+

  • Levitiko 16:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 “Wansembe amene adzadzozedwa+ ndi kupatsidwa mphamvu* kuti atumikire monga wansembe,+ kulowa m’malo+ mwa bambo ake, aziphimba machimo ndipo azivala zovala za nsalu.+ Zovala zimenezo ndi zopatulika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena