Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 4:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Kenako iye anati: “Iponye pansi.” Anaiponya pansi ndipo inasanduka njoka.+ Pamenepo Mose anayamba kuthawa.

  • Ekisodo 4:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Kenako Yehova anamuuzanso kuti: “Lowetsa dzanja lako m’malaya pachifuwa.” Choncho Mose analowetsa dzanja lake m’malaya. Koma politulutsa, dzanja lakelo linali litachita khate, ndipo linaoneka loyera kwambiri ngati chipale chofewa.+

  • Ekisodo 4:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Komabe ngati sakakhulupirira zizindikiro ziwirizi ndi kumvera mawu ako,+ ukatenge madzi a mumtsinje wa Nailo n’kuwathira panthaka youma. Ndipo madziwo, amene ukatenge mumtsinje wa Nailo, adzasanduka magazi panthakapo. Ndithu adzasanduka magazi.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena