Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 9:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pamenepo Mose ndi Aroni analowa m’chihema chokumanako, kenako anatulukamo n’kudalitsa anthuwo.+

      Atatero, ulemerero wa Yehova+ unaonekera kwa anthu onse,

  • Numeri 6:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 “Lankhula ndi Aroni ndiponso ana ake kuti, ‘Muzidalitsa+ ana a Isiraeli motere:

  • Yoswa 22:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Atatero, Yoswa anawadalitsa+ n’kuwauza kuti azipita kumahema awo.

  • 1 Mafumu 8:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kenako mfumu inatembenuka n’kuyang’ana anthuwo. Ndiyeno inayamba kudalitsa+ mpingo wonse wa Isiraeli. Pamenepo n’kuti mpingo wonse wa Isiraeli utaimirira.

  • 2 Mbiri 30:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Pomalizira pake ansembe achilevi anaimirira n’kudalitsa+ anthuwo, ndipo mawu awo anamvedwa moti pemphero lawo linafika kumwamba, kumalo oyera okhala Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena