Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 30:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 “Upange guwa lansembe la zofukiza.+ Ulipange ndi matabwa a mthethe.

  • Salimo 141:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pemphero langa likhale lokonzedwa ngati zofukiza+ pamaso panu,+

      Mapembedzero anga akhale ngati nsembe yambewu yamadzulo.+

  • Luka 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Khamu lonse la anthu linali kupemphera panja, pa ola lopereka nsembe zofukizalo.+

  • Chivumbulutso 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Atatenga mpukutuwo, zamoyo zinayi ndi akulu 24 aja+ anagwada ndi kuwerama pamaso pa Mwanawankhosa. Aliyense wa iwo anali ndi zeze woimbira+ ndi mbale yagolide yodzaza ndi zofukiza. Zofukizazo+ zikuimira mapemphero+ a oyera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena