Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 7:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Pempha chizindikiro kwa Yehova Mulungu wako.+ Chikhoza kukhala chozama ngati Manda kapena chachitali ngati malo okwera.”

  • Mateyu 12:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Poyankha iye anawauza kuti: “M’badwo woipa ndi wachigololo+ ukufunitsitsabe chizindikiro. Sudzapatsidwa chizindikiro chilichonse koma chizindikiro cha mneneri Yona chokha.+

  • Yohane 6:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndiyeno iwo anamufunsa kuti: “Ndiye inuyo muchita chizindikiro+ chotani, kuti ife tichione, ndi kukukhulupirirani? Muchita ntchito yotani?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena