Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 6:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tsopano Amuramu anatenga Yokebedi, mlongo wa bambo ake, kukhala mkazi wake.+ Ndipo Yokebedi anam’berekera Amuramu, Aroni ndi Mose.+ Amuramu anakhala ndi moyo zaka 137.

  • Numeri 26:59
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 59 Mkazi wa Amuramu anali Yokebedi,+ mwana wa Levi, amene mkazi wake anam’berekera ku Iguputo. Yokebedi anaberekera Amuramu ana awa: Aroni, Mose ndi mlongo wawo Miriamu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena