Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 17:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mwana aliyense wamwamuna amene wakwanitsa masiku 8 azidulidwa+ m’mibadwo yanu yonse. Aliyense wobadwira m’nyumba yanu ndi aliyense wosakhala mbewu yanu koma wogulidwa ndi ndalama kwa mlendo azidulidwa.

  • Genesis 17:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndiyeno Abulahamu anatenga mwana wake Isimaeli ndi amuna onse obadwira m’nyumba yake, ndi aliyense amene anamugula ndi ndalama zake, komanso mwamuna aliyense wa m’nyumba ya Abulahamu. Anawadula khungu lawo la kunsonga tsiku lomwelo, monga mmene Mulungu anamuuzira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena