Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 6:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Chotero ndidzakutengani kukhala anthu anga,+ ndi kukusonyezani kuti ndine Mulungu.+ Inuyo mudzadziwadi kuti ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndidzakutulutsani mu Iguputo, ndi kukuchotserani goli lawo.+

  • Numeri 16:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Ndiyeno Mose anati: “Mudziwira izi kuti Yehova ndiye anandituma kuti ndichite zonsezi,+ ndiponso kuti si za mumtima mwanga ayi:+

  • Salimo 77:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mwatsogolera anthu anu ngati nkhosa,+

      Kudzera mwa Mose ndi Aroni.+

  • Yesaya 63:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iwo anayamba kukumbukira masiku akale, masiku a Mose mtumiki wake, ndipo anafunsa kuti: “Kodi amene anawatulutsa m’nyanja+ pamodzi ndi abusa a anthu ake uja, ali kuti?+ Ali kuti amene anaika mzimu wake woyera mwa iye?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena