Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 14:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiyeno Yehova analankhula ndi Mose kuti: “Kodi anthu awa apitiriza kundinyoza kufikira liti?+ Kodi adzayamba liti kundikhulupirira pambuyo pa zizindikiro zonse zimene ndachita pakati pawo?+

  • 2 Mafumu 17:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma iwo sanamvere. M’malomwake anaumitsa makosi awo,+ ngati mmene makolo awo anaumitsira makosi awo. Makolo awowo sanasonyeze chikhulupiriro+ mwa Yehova Mulungu wawo.

  • Salimo 78:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iwo sanasunge pangano la Mulungu,+

      Ndipo anakana kutsatira chilamulo chake.+

  • Salimo 81:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Haa! Zikanakhala bwino ngati anthu anga akanandimvera,+

      Zikanakhala bwino ngati Isiraeli akanayenda m’njira zanga.+

  • Salimo 106:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Koma mofulumira anaiwala ntchito zake,+

      Iwo sanayembekezere malangizo ake.+

  • Luka 16:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Koma iye anamuuza kuti, ‘Ngati sakumvera Zolemba za Mose+ ndi Zolemba za aneneri, sangathekebe ngakhale wina atauka kwa akufa.’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena