Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 27:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mumangirenso Yehova Mulungu wanu guwa lansembe kumeneko, guwa lansembe lamiyala. Musaseme miyalayo ndi chipangizo chilichonse chachitsulo.+

  • Yoswa 8:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Anamanga guwalo mogwirizana ndi zimene Mose mtumiki wa Yehova analamula ana a Isiraeli, monga mwa zolembedwa m’buku la chilamulo+ cha Mose, zimene zimati: “Guwa lansembe la miyala yathunthu, yosasema ndi chipangizo chachitsulo.”+ Ndipo iwo anaperekerapo kwa Yehova nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena