Levitiko 22:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Ng’ombe kapena nkhosa yokhala ndi chiwalo chimodzi chachitali kwambiri kapena chachifupi kwambiri kuposa chinzake,+ mungaipereke monga nsembe yaufulu, koma Mulungu sadzailandira mukaipereka pokwaniritsa lonjezo lanu. Deuteronomo 12:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Nsembe zanu zopsereza+ ndi nsembe zina, zopereka zanu za chakhumi,*+ chopereka chochokera m’manja mwanu,+ nsembe zanu za lonjezo,+ nsembe zanu zaufulu,+ ana oyamba kubadwa a ng’ombe ndi a nkhosa zanu,+ zonsezi muzidzazibweretsa kumalo amenewo.
23 Ng’ombe kapena nkhosa yokhala ndi chiwalo chimodzi chachitali kwambiri kapena chachifupi kwambiri kuposa chinzake,+ mungaipereke monga nsembe yaufulu, koma Mulungu sadzailandira mukaipereka pokwaniritsa lonjezo lanu.
6 Nsembe zanu zopsereza+ ndi nsembe zina, zopereka zanu za chakhumi,*+ chopereka chochokera m’manja mwanu,+ nsembe zanu za lonjezo,+ nsembe zanu zaufulu,+ ana oyamba kubadwa a ng’ombe ndi a nkhosa zanu,+ zonsezi muzidzazibweretsa kumalo amenewo.