Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 29:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Zonsezi uziike m’manja mwa Aroni ndi m’manja mwa ana ake,+ ndi kuziweyulira* uku ndi uku monga nsembe yoweyula yoperekedwa kwa Yehova.+

  • Levitiko 8:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Atatero anaika zonsezi m’manja mwa Aroni ndi m’manja mwa ana ake n’kuyamba kuziweyula* uku ndi uku monga nsembe yoweyula yoperekedwa kwa Yehova.+

  • Levitiko 9:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Koma Aroni anaweyula*+ cha uku ndi uku ngangazo ndi mwendo wakumbuyo wa kudzanja lamanja pamaso pa Yehova, monga mmene Mose analamulira.

  • Numeri 6:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tsopano wansembeyo aweyulire* zinthuzo uku ndi uku monga nsembe yoweyula kwa Yehova.+ Zinthuzi zipite kwa wansembeyo ngati mphatso yopatulika, limodzi ndi nganga+ ya nsembe yoweyulayo, komanso mwendo umene aupatula kuti ukhale chopereka.+ Pambuyo pake yemwe anali Mnaziriyo angathe kumwa vinyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena