Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 10:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Chotero Yehova anauza Mose kuti: “Tambasula+ dzanja lako ndi kuloza dziko la Iguputo, kuti dzombe ligwe m’dziko lonselo ndi kudya zomera zonse za m’dzikomo, chilichonse chimene matalala anasiya.”+

  • Miyambo 30:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Dzombe+ lilibe mfumu koma limauluka lonse litagawikana m’magulumagulu.+

  • Yesaya 33:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Zinthu zimene anthu inu munalanda+ ena zidzasonkhanitsidwa ngati mphemvu zikasonkhana pamodzi, ndiponso ngati chigulu cha dzombe chimene chikukhamukira kwa munthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena