Ekisodo 22:31 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 31 “Inuyo muzikhala anthu oyera pamaso panga+ ndipo musadye nyama imene yaphedwa ndi chilombo kuthengo.+ Imeneyo muziponyera agalu.+ Levitiko 20:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 “‘Choncho mudzipatule monga anthu oyera,+ chifukwa ine ndine Yehova Mulungu wanu. Levitiko 20:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Mukhale oyera kwa ine,+ chifukwa ine Yehova ndine woyera.+ Ine ndikukupatulani kwa anthu a mitundu ina kuti mukhale anthu anga.+ Numeri 15:40 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 40 Ndakupatsani lamulo limeneli kuti muzikumbukira ndi kusunga malamulo anga onse, ndi kukhaladi oyera kwa Mulungu wanu.+ Deuteronomo 7:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Pakuti ndinu anthu oyera kwa Yehova Mulungu wanu.+ Yehova Mulungu wanu anakusankhani kuti mukhale anthu ake, chuma chake chapadera, mwa anthu onse okhala padziko lapansi.+
31 “Inuyo muzikhala anthu oyera pamaso panga+ ndipo musadye nyama imene yaphedwa ndi chilombo kuthengo.+ Imeneyo muziponyera agalu.+
26 Mukhale oyera kwa ine,+ chifukwa ine Yehova ndine woyera.+ Ine ndikukupatulani kwa anthu a mitundu ina kuti mukhale anthu anga.+
40 Ndakupatsani lamulo limeneli kuti muzikumbukira ndi kusunga malamulo anga onse, ndi kukhaladi oyera kwa Mulungu wanu.+
6 Pakuti ndinu anthu oyera kwa Yehova Mulungu wanu.+ Yehova Mulungu wanu anakusankhani kuti mukhale anthu ake, chuma chake chapadera, mwa anthu onse okhala padziko lapansi.+