Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 1:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “‘Koma ngati akupereka mbalame kuti ikhale nsembe yake yopsereza kwa Yehova, azipereka njiwa+ kapena ana a nkhunda.+

  • Levitiko 14:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 “Kenako wansembe azipereka mmodzi mwa ana a njiwa kapena m’modzi mwa ana a nkhunda, malinga ndi zimene munthuyo angakwanitse.+

  • Levitiko 14:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Ndiyeno kuti achite mwambo woyeretsa nyumbayo, azitenga mbalame ziwiri,+ nthambi ya mtengo wa mkungudza,+ ulusi wofiira kwambiri+ ndi kamtengo ka hisope.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena