Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 72:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Adzamvera chisoni munthu wonyozeka ndi wosauka,+

      Ndipo adzapulumutsa miyoyo ya anthu osauka.+

  • Miyambo 17:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Wonyoza munthu wosauka amanyoza amene anam’panga.+ Amene amasangalala ndi tsoka la wina sadzalephera kulangidwa.+

  • Miyambo 22:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Munthu wolemera ndiponso munthu wosauka n’chimodzimodzi.+ Amene anapanga onsewa ndi Yehova.+

  • Luka 6:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Pamenepo anakweza maso ake ndi kuyang’ana ophunzira ake, ndipo anawauza kuti:+

      “Odala ndinu osaukanu,+ chifukwa ufumu wa Mulungu ndi wanu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena