Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 31:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kodi amene anandipanga m’mimba si amene anapanganso iyeyo?+

      Kodi si mmodzi yemweyo amene anatipanga tonsefe m’mimba?

  • Yobu 34:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Alipo amene sanakonderepo akalonga,

      Ndipo saganizira kwambiri wolemekezeka kuposa wonyozeka,+

      Chifukwa onsewo anapangidwa ndi manja ake.+

  • Machitidwe 17:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndipo kuchokera mwa munthu mmodzi+ anapanga mtundu wonse wa anthu,+ kuti akhale padziko lonse lapansi.+ Iye anakhazikitsa nthawi zoikidwiratu+ komanso anaika malire achikhalire a malo oti anthu azikhala.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena