Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 15:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “‘Ndiyeno munthu akachira nthenda yake yakukhayo, pazipita masiku 7 kuti akhale woyera,+ kenako azichapa zovala zake ndi kusamba madzi otunga kumtsinje,+ ndipo iye azikhala woyera.

  • Levitiko 15:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pa tsiku la 8 azitenga njiwa ziwiri+ kapena ana awiri a nkhunda ndipo azibwera nazo pamaso pa Yehova, pakhomo la chihema chokumanako, ndi kupereka mbalamezo kwa wansembe.

  • Numeri 12:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndiyeno Yehova anauza Mose kuti: “Kodi bambo ake akanam’lavulira+ malovu kumaso, sakanakhala wonyazitsidwa masiku 7? Choncho m’tulutseni+ akakhale kunja kwa msasa masiku 7,+ pambuyo pake mum’landire mumsasamo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena