Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 18:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Motero inu muzisunga mfundo zanga ndi zigamulo zanga.+ Ndipo aliyense wa inu, kaya ndi nzika kapena mlendo wokhala pakati panu,+ musachite chilichonse cha zinthu zonyansa zimenezi.

  • Salimo 105:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Anachita zimenezi kuti asunge malangizo ake,+

      Ndi kusunga malamulo ake.+

      Tamandani Ya, anthu inu!+

  • Salimo 119:80
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  80 Mtima wanga usunge malangizo anu mosalakwitsa kanthu,+

      Kuti ndisachite manyazi.+

  • Mlaliki 12:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Poti zonse zanenedwa, mfundo yaikulu ndi yakuti: Opa Mulungu woona+ ndi kusunga malamulo ake+ chifukwa zimenezi ndiye zimene munthu ayenera kuchita.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena